Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 345 ATATE, ndipempha

  1. Home   »  
  2. Hymn 345 ATATE, ndipempha

Hymn 345 ATATE, ndipempha

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 345 ATATE, ndipempha

 

ATATE, ndipempha
Tsopano mundimvere,
Ndipempha kuti mundithandize.

Ine ndili munthu
Wochimwa pansi pano,
Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.

Ndalema ndathodwa
Ndi zinthu zapadziko,
Zakhalatu goli londimanga.

Yesu Mfumu Inu
Mumandiuza kuti:
“Pemphera, ndipo udzalandira.”

Ndipempha, Ambuye,
Mundidzaze n’chikondi,
Mtima wangawu ukukondeni.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version