Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 345 ATATE, ndipempha

  1. Home   »  
  2. Hymn 345 ATATE, ndipempha

Hymn 345 ATATE, ndipempha

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 345 ATATE, ndipempha

 

ATATE, ndipempha
Tsopano mundimvere,
Ndipempha kuti mundithandize.

Ine ndili munthu
Wochimwa pansi pano,
Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.

Ndalema ndathodwa
Ndi zinthu zapadziko,
Zakhalatu goli londimanga.

Yesu Mfumu Inu
Mumandiuza kuti:
“Pemphera, ndipo udzalandira.”

Ndipempha, Ambuye,
Mundidzaze n’chikondi,
Mtima wangawu ukukondeni.

Post navigation

Previous: Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
Next: Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version