Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version