Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 315 YENDANI munjira yake,
Next: Hymn 317 UKATHA moyo wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version