Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 315 YENDANI munjira yake,
Next: Hymn 317 UKATHA moyo wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version