Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 294 POYESEDWA ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 294 POYESEDWA ine

Hymn 294 POYESEDWA ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 294 POYESEDWA ine

 

POYESEDWA ine
Yesu mudzetu,
Mundipempherere
Ndisachimwetu.
Mukaona kuti
Ndilefukatu,
Mbuye mndilimbitse
Nazo mphamvutu.

Ndi zapansi pano
Ndikokedwadi,
Koma ndi chisoni
Mndiphunzitsedi;
Ndisaiŵalire
Za Getsemane,
Pena mtanda wanu
Yesu Mbuye ’Nu.

Mukandipweteka,
Ndipirirapo:
Nsembe yanga ndiyo,
Landirani ’yo.
Ndikachita mantha Sindithaŵa ’yi:
Mtima udzalimba,
Ndidzaima nji!

Pakumalizidwa
Moyo wangawu,
Pomwalira ine,
Mudze Mbuyetu.
Ndidzadzipereka
M’manja mwanumo:
Mpulumutsi Yesu
Mndilandireko.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version