Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

 

KUNALI munthu ku Yeriko,
Dzina lake Zakeyu;
Anali munthu wamkulu,
Wokhometsa misonkho.

(M) Kunali Zakeyu,
(O) Ku Yeriko,
(M) Nafunafuna,
(O) Kuwona Yesu,
(M) Koma chifukwa,
(O) Cha khamulo,
Anakwera mumtengo.

Paulendowo Ambuyeyo,
Anafika pamtengo;
Nayang’ana m’mwamba muja,
Anawona Zakeyu,

Ambuye Yesu nanenadi,
“Fulumira nutsike;
Lero lino ndiyenera,
Kukhala m’nyumba mwako.”

Zakoyuyo mofulumira,
Anatsika mumtengo,
Anam’tenga Mbuye Yesu,
Kuti akam’chereze,

Anadandauladi ena,
“Ambuye wachitanji?
Bwanji Iye analowa,
M’nyumba ya wochimwayo?”

Zakeyuyo pakumva ichi,
Anawuza Ambuye:
“Theka la chuma changacho,
Ndidzapatsa osowa.”

Leronso chipulumutsochi,
Chagwera m’nyumba yathu;
Tilape zoipa zathu,
Kutí tipulumuke.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version