Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
Next: Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version