Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version