Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 118 PANALI munthu amene,

  1. Home   »  
  2. Hymn 118 PANALI munthu amene,

Hymn 118 PANALI munthu amene,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 118 PANALI munthu amene,

 

PANALI munthu amene,
Analimbana ndi mngelo;
Kufikira mbandakucha:
“Sindidzakusiya.”

(M) Ndipo mngelo anati:
(O) “Yakobo iwe, ndisiye;
Kunja kuli kucha, ndisiye,
“Sindidzakusiya!”

Pomwepo mngelo ‘nafunsa:
“Dzina ndi yani?”
“Yakobo,’
“Dzina ndi yani?”
“Yakobo,
Sindidzakusiya.”

Ndipo Mulungu afuna,
Tigwire ntchito yakeyo;
Yolimbana ndi zoipa,
Zodetsa m’mtimamo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version