Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

 

MUNASIYATU dziko lanulo,
E, chifukwa cha íne;
Ndi ku Betlehemuko,
Pakubadwa Inu,
M’nyumba zawo nakukanani.

Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga;
Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga.

Akumwambako nayimbitsatu,
Kukulemekezaní;
Koma monga mwana,
M’dziko munabadwa,
Munadzíchepetsadi.

Nyama za mthengo ndi mbalamezo,
Zili namo mogonamo;
Koma Mwana Mlungu,
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.

Munadzera ndi mawu amoyo,
Akupulumutsa anthu;
Anakaníza,
Anasautsa,
Anapachika Inu.

Mmene mubwera kutiŵeruza,
Ndi angelo oyimbira;
Mundiitane,
Muti, “Idza ‘we,
Khala nane Kumwamba.”

Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso;
Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso.

Post navigation

Previous: Hymn 38 ANGELO ayimba,
Next: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version