Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

 

NDI mitima yokondwera,
Mbuye wathu tiyamika.

E, chifundo chake chonse,
Ndi chosatha nthaŵi zonse.

Dzina lake tibukitsa,
Mlungu ndiye yekhayekha.

Mphamvu yake inalenga,
Dziko lonse ndi kumwamba.

Anatsogolera kale,
M’chipululu anthu ake.

Ndi chifundo atipenya,
Ife anthu osawuka.

Amaŵeta nyama zonse,
Zingasoŵe kanthu konse.

Tiimbire Mlungu wathu,
Waulemu ndi wamkulu.

Tithaŵire kwa Mulungu,
Ndiko tikapeze moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 10 TSOPANO linoli,
Next: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version