Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

 

NDI mitima yokondwera,
Mbuye wathu tiyamika.

E, chifundo chake chonse,
Ndi chosatha nthaŵi zonse.

Dzina lake tibukitsa,
Mlungu ndiye yekhayekha.

Mphamvu yake inalenga,
Dziko lonse ndi kumwamba.

Anatsogolera kale,
M’chipululu anthu ake.

Ndi chifundo atipenya,
Ife anthu osawuka.

Amaŵeta nyama zonse,
Zingasoŵe kanthu konse.

Tiimbire Mlungu wathu,
Waulemu ndi wamkulu.

Tithaŵire kwa Mulungu,
Ndiko tikapeze moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 343 Auke,
  • Hello world!
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version