Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,

Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,

 

TAMANI mphamvu ya Yesu,
Angelo agwade;
Angelo agwade;
Tulutsanitu korona,

Mumveke, mveke, mveke,
Mveke, mveke, mveke,
Mveke Mbuyeyo!

Inu osankhidwa ake,
Owomboledwa ’Nu,
Owomboledwa ’Nu,
Tamani Mpulumutsiyo,

Anthu onse ndi mitundu
Pa dziko linotu,
Pa dziko linotu,
Am’lemekeze Mfumuyo.

Tifuna kuti komweko
Tikam’gwadire ’Ye;
Tikam’gwadire ’Ye;
Tidzayimba kosaleka.

Post navigation

Previous: Hymn 94 KHAMULO liliko
Next: Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 479 Munanena mulandira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version