Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

 

TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
Yakuyamika Mbuye wathuyo;
Mtendere wake tiufunadi,
Titapemphera tinke kwathuko.

Titanka kwathu mkhale nafeko,
Tikufunani Yesu Mbuyathu;
Musunge ife nthaŵi zonsezo,
Mutiyeretse m’mtima mwathu mbuu!

Usiku uno mutisungedi,
Khalani m’fupi m’nyumba mwathumo;
Mamaŵanso mudzatidzutse nji!
Kuti tigwire ntchito zathuzo.

Mtitsogolere nthaŵi zonsezo;
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo,
Sitidzaopa kanthu kena ’yi.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version