Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 215 Choka, choka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version