Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

  1. Home   »  
  2. Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

 

TIIMBE ndi kulalikira
Mthenga wa chikondicho
Anamva Mlungu m’Mwambamo
Kulira kwathu pansipa.

(Ndikhulupirira Yesu
Wobadwira m’kholamo;
Iye ndiye Mfumu yathu,
Timtame nthaŵi zonse.)

Kwa ife lero anabadwa
Mwana wa Mariyayo,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma
Mwini dziko lonseli.

Anadza nazo mphatso zake
Anatikonzeratu; Anatitseguliradi
Pakhome pa Ufumuwo.

Ambuye takutamandani
Tsiku lakubadwali,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Tiseke tonsefe.

A! Yesu Mbuye wakuyera,
Munagona m’kholamo;
Mudzikonzere leronso
Mogona m’mtima mwangamu.

Ulemerero m’Mwambamwamba
Ndi mtendere pansipa;
Tiimbe nafe nyimboyi,
Timyamikire Mbuyathu

(Yesu ndiye Mfumu,
Yesu ndiye Mfumu!
Ndikhulupirira Yesu wobadwira m’kholamo.)

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version