Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

  1. Home   »  
  2. Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

 

M’MAŴA tizifesa
Mbewu zakukoma,
Msana ndi usiku
Tizifesa momwe.
Nyengo yamasika
Tidzatema m’munda,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Ndi zipatsozo
Ndi zipatsozo
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tizifesa m’dzuŵa
Tizifesa m’mthunzi,
Sitiopa ife
Mtambo ndi chisanu.
Athatu masika
Ntchitozi zidzatha;
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tingolira kaya,
Koma tidzafesa
Mbewu za Ambuye;
Ntchitoyo nja Yesu.
Adzachotsa msozi,
Adzatilandira,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Post navigation

Previous: Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
Next: Hymn 444 YEMWE afesa nalira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version