Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

 

TAMVA mawu omwewo,
Atitu Yesuyo;
Mpulumutsi ndiyedi,
Yesuyo, Yesuy0.
Pita m midzi monsemo,
Dziko lonse limvetu;
Pita iwe konseko0,
Mveratu Mbuyeyo.

Imbadi za lyeyo,
Amvetu anthuwo;
Kuti Yesu ‘nafadi,
Kalero, kalero.
Atikonda ifetu,
Natifera indedi;
Kuchotsera tchimoli,
Yesuyo, Yesuyo.

Bukitsanı mawuns0,
Konseko, konseko
Kayitane anthuwo,
Ponsepo, ponsepo.
Kodi wina samvatu?
Pitako, pitako we
Angofuna onsewo,
Yesuyo, Yesuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version