Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

 

MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Nkana ine ndimalakwa,
Koma ndinu moyo wanga;
Mbuye, mkhale ndine.

Ndine mlendo pansi pano,
Msanditaye m’dzanja lanu,
Mundisunge mwana wanu;
Mbuye, mkhale ndine.

Munafera ine kale
Kuti mukandimasule,
Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.

Mundidzaze ndi chikondi,
Mndiyeretse m’mtima monse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuye, mkhale ndine.

Imfa ikandifikira,
Inu ndidzakangamira
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mbuye, mkhale ndine.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 450 Koma usalole

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version