Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version