Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

  1. Home   »  
  2. Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

 

MWAKHULUPIRIRADI
Yesu Ambuyathu;
Muli nazo zakezo,
Zidzatu zinanso.
Mlungu wachisomocho
Mbuye wathu ndiye,
Ati zinthu zonsezo
Nzathu mwa Iyeyo.

(Zina ndi zinanzo
Zidza kwa ifedi,
Inde mtima wakewo
Uli wokomadi.)

Mwamva Yesu m’mtimamo,
Adzanso kaŵiri,
M’mene ali nanutu
Muli ndi Chimwemwe.
Ntchito zachifundozi
Iye watha izi,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Naye tikhalebe.

Mwamva Mzimu wakewo,
Zake zimvekanso
Kugwa ngati mvulayo
Yachisomo chake.
Mzimu ndiye mphamvudi
M’moyo mwathu muno,
Mpaka tidzafikako
Komwe kuli Yesu

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version