Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

 

MU ZONSE abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa anthu ake,
Zomwe iwo akuzisowa.

Akhrisitu pamavuto tiyeni timulemekeze,
Pamtendere tiyeni timulemekeze.
Maso ake ali pa anthu,
Okhala m’dziko lapansi.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kuveka anthu ake,
Ngakhale nyama zakuthengo.

Mu zonse abale yamikani,
Mulungu ndi wamkulu,
Adziwa kupatsa mphatso zake,
Ngakhalenso kwa tiŵanato.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version