Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

  1. Home   »  
  2. Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

 

INE ndili ndi manyazi
Kuti kale lomwelo
Ndinanyoza kudza komwe
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
Ndati, Sindimfuna `yi.

Koma Iye wandipeza;
Ndamuona m`mtandamo,
Mwa kufera ine momwe;
Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mbuye, ndikufunani.

Nsiku zonse kwanja kwake
Kunandithandizatu,
Kunandichiritsa mtima;
Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Ndinu Mbuye wangatu.

Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version