Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

 

KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Pochimwa anthu onsewo
Nja Mlungu nzeruyi;
Adamu wachiŵiriyo
Wathetsa tchimoli.

Thupi la mwazi wathu ’li
Lochimwa kalelo,
Labweranso ku nkhondoyi,
Laposa monsemo.

Choposa nalo thupilo
Chikhale momwemu,
Chiyeretsetsa m’katimo,
Ndi Mulungu Iyeyu.

Anatikondakonda ’Ye,
Ndi Mlungu Iyeyo,
Anatifera anthu ’fe
Ndi Mulungu Iyenso.

Ndi m’munda muja chete, phee!
Pamtanda pati njo!
Anaphunzitsa’bale ’fe
Titero ifenso.

Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version