Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

 

USANABADWE, Yeremiya,
Ine ndinakudziwa;
Ndipo ndinakupatula,
Kuti ukhale mneneri.

Ulalike mawu anga Yeremiya,
Pita ukalalikire
Mawu anga;
Mawu anga Yeremiya.

“Usaopetu nkhope zawo,
Ine ndili ndi iwe;
Kuti ndikulanditsetu,
Iweyo,” ati Yehova.

Usaganize ndiwe mwana,
Iwe udzanka konse;
Kumene ndidzakutuma,
Kuti ukalalikire.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version