Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 112 ELISA mneneri,

  1. Home   »  
  2. Hymn 112 ELISA mneneri,

Hymn 112 ELISA mneneri,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 112 ELISA mneneri,

 

ELISA mneneri,
Wachita zamphamvu;
Kuyandamitsa nkhwangwayo,
Pa Yolodani’po.

(M) Nkhwangwayo,
(O) Ndiyobwereka,
Nalira mnyamatayo;
Popeza ndiyobwereka,
Pa Yolodanipo.

Elisa mneneri,
Natenga kamtengo;
Naponya pamadzi paja,
Nkhwangwa niyandama.

Mulungu wamphamvu,
Natuma Mwana ‘ke;
Kuti atifere ife,
Kutipulumutsa.

Nanga ife lero,
Kodi takonzeka;
Kusiya machimo athu,
Kutsata Yesuyo?

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version