Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
Dziko lonse nla Mulungu
Kuti limbalire dzinthu;
M’munda zonse zimamera
Zakukoma ndi zoipa;
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakwima;
Mutilole, Mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu zanu.