Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

 

M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
Msunge zakuonazo,
Mudalitse anthu onse
Ndi chifumu chanucho.

MMbwere Yesu Mwini moyo,
Ukuletu ’lemuwo;
Gonjetsani anthu onse,
Mpatsenso mtenderewo.

Mbwere Mzimu Wakuyera,
Mutitsitsimutseko;
Muthaŵitse mdima wonse,
Muŵalitse m’mtimamo.

Anthu onse taukani,
Imbirani Mlunguyo;
Zichuluke zomtamanda
Pansi ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version