Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

  1. Home   »  
  2. Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

 

ANTHU akum’maŵa
Nanka msangako,
Nzeru ’nali nazo,
Nafatsansowo;
Nanka kuli Mwana
Anabadwayo;
Anatsogozedwa
Ndi nyenyeziyo.

Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Nagwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.

Mu ulemerero,
Yesu m’Mwambamo
Muli eni ake;
Anthu onsewo
Osadziŵa konse,
Akutalinso,
Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.

Akukhala kunja,
Osokeranso,
M’ŵaŵalire Mbuye,
Asagone’wo;
Amumdima omwe,
Olemedwanso,
Mtsogoleri wawo
Ndi nyenyeziyo.

Paulendo wathu
Tili pansipa,
Muŵalire tonse
Tili m’njiramo;
Mutitsogolere
Anthu tonsefe,
Mutifitse tonse
Ndi nyenyeziyo.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version