Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

 

YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Upeze moyo;
Chuma cha dziko chidzatha,
Yang’ana kwa Yesu.

Poyang’ana kwa Yesu Mbuye,
Pakuwona pamtanda wake,
Moyo ulipo.

Yesu alira pamtanda,
Kulilira ‘fe;
Kuti tilape zoipa,
Zomwe tichitazi.

Ambuye anatifera,
Pamtanda paja;
Kuti tikapeze moyo,
Kumwamba kwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
Next: Hymn 405 POLENGA dzikoli

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version