Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,

Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,

 

LERO mwatipatsa moyo,
Wadza mdima, kwada bii;
Mtigonetsetu usiku,
Mchotse zakuipazi.
Yesu mutisunga ife;
Tidzakhulupirabe.
Yesu mutisunga ife;
Tidzakhulupirabe.

Ndife anthu aulendo,
Tili ndi adaniwo;
M’manja mwanu mtigonetse,
Mtichotsere manthawo.
Ndipo pakumuka ife,
Kwanu tidzapumabe.
Ndipo pakumuka ife,
Kwanu tidzapumabe

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version