Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

 

M’DZIKO lino tikhalamo
Utibvuta moyo,
Koma dziko la mtendere
Lili kwa Mulungu.

Watitsogolera Mbuye,
Komwe kwa Atate,
Ndimo tidzatsata naye
Moyo wathu wonse.

Ndi tsopano tilindira
M`dziko lathu lino;
Ntchito atipatsa Mlungu,
Tizigwira bwino.

Ngati zakuipa zathu
Zikatisautsa,
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Atipulumutsa.

Timpemphere kutipatsa
Mtima watsopano,
Kutithandizira kunka
Paulendo uno.

Post navigation

Previous: Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
Next: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version