Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

 

M’DZIKO lino tikhalamo
Utibvuta moyo,
Koma dziko la mtendere
Lili kwa Mulungu.

Watitsogolera Mbuye,
Komwe kwa Atate,
Ndimo tidzatsata naye
Moyo wathu wonse.

Ndi tsopano tilindira
M`dziko lathu lino;
Ntchito atipatsa Mlungu,
Tizigwira bwino.

Ngati zakuipa zathu
Zikatisautsa,
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Atipulumutsa.

Timpemphere kutipatsa
Mtima watsopano,
Kutithandizira kunka
Paulendo uno.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version