Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

  1. Home   »  
  2. Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

 

NDIMAYENDA paulendo
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako.

Ichi chindisangalatsa
M’mene nkhondo indigwira,
M’mene nsoni zazikulu
Zimanditsatira;
Mtima ukhazika m’mene
Kwathu kuja ndikumbuka
Kuti Mlungu ali ndine,
Andisungako.

Mbuye andipeza lero,
Andikonda, andisunga;
Adzapitikitsa mdani
Akamandibvuta.
E, ulendo wanga utha,
Tsono ine ndimwalira;
M’mene ndidzafika kwawo
And’landirako.

Komwe ndi chimwemwe ine
N’dzaonana ndi Atate,
N’dzagwadira ndi kumtama,
Amandikondabe.
Sakandisautsa kanthu
M’dziko lija lakukoma;
Adzandidalitsa Yesu,
Ndidzakondwako.

Post navigation

Previous: Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
Next: Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version