Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

  1. Home   »  
  2. Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

 

NDIMAYENDA paulendo
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako.

Ichi chindisangalatsa
M’mene nkhondo indigwira,
M’mene nsoni zazikulu
Zimanditsatira;
Mtima ukhazika m’mene
Kwathu kuja ndikumbuka
Kuti Mlungu ali ndine,
Andisungako.

Mbuye andipeza lero,
Andikonda, andisunga;
Adzapitikitsa mdani
Akamandibvuta.
E, ulendo wanga utha,
Tsono ine ndimwalira;
M’mene ndidzafika kwawo
And’landirako.

Komwe ndi chimwemwe ine
N’dzaonana ndi Atate,
N’dzagwadira ndi kumtama,
Amandikondabe.
Sakandisautsa kanthu
M’dziko lija lakukoma;
Adzandidalitsa Yesu,
Ndidzakondwako.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version