Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

  1. Home   »  
  2. Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

 

NDIDZE pafupi pa
Mlungu wanga,
Ngakhale pamtanda
Mundikweza;
Koma ndiimbabe
Mbuye mndikhalitse,
Mbuye mndikhalitse,
M’fupi Ndinu.

Ngakhale kuthengo
Ndasokera,
M’mdima ndigonapa
E, pamwala;
Koma m’kulotako
Ndiyandikizanso,
Ndiyandikizanso
M’fupi Ndinu.

Pajapo ndipenya
Pokwerapo,
Angelo atsika
Kumwambako,
Ndiwo akodola
Kuti ndikabwere,
Kuti ndikabwere
M’fupi Ndinu.

Tsopano poukanso
Wokondwatu,
Ndipeza pomwepo
Pali Mlungu;
Ndipo masautso
Andisendezanso,
Andisendezanso,
M’fupi Ndinu.

Pena pakufadi,
N’kwera m’Mwamba,
Dzuŵa ndi nyenyezi
Zitsalira;
Pomwe ndiimbanso,
Ndidza pafupi pa,
Ndidza pafupi pa
Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 301 MBUYE, ndapangana
Next: Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version