Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version