Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
Next: Hymn 274 YESU and’itana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version