Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 239 TILI ndi mtendere

  1. Home   »  
  2. Hymn 239 TILI ndi mtendere

Hymn 239 TILI ndi mtendere

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 239 TILI ndi mtendere

 

TILI ndi mtendere
Wopambanatu,
Monga ngati mtsinje
Mumitimamo;
Koma mtsinje uno
Umayenda phee,
Nthaŵi zonse mtima
Nutonthozabe.

Tikakhulupira
Mlungu wathuyo,
Tidzaona mwayi
Ndi mtenderewo.

Dzanja la Mulungu
Litisunga nji!
Nkhondo ya Satana
Sitiopa ’yi.
Zaphokoso zonse
Ndi zoopsyazo
Sizibvuta mtima,
Siziloŵamo.

Masauko athu
Ndi zokondwazo,
Azilola zonse
Ndi Atatewo.
Pokhulupirira
Tidzapezabe
Kuti mtima wake
Utikonda ’fe.

YESU ndiye Mbuye wanga,
Ndamva Mawu akewo
Andilandira ine,
Nandipulumutsatu.
Mwalembedwa mukalata
Mawu ake omwewo,
Kuti iwo akumvera
Akalandiridwatu.

Ndinakahala wakuipa, Ndinamkana kalelo;
Koma Yesu waiŵala
Mphulupulu zangazo.

Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu
Mau ake olembedwa
Mukalata mwakemo.

Mumvetu abwenzi athu,
Musakanirire ’yi;
Yesu aitana inu,
Zalembedwa zomwezi.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version