Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

  1. Home   »  
  2. Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

 

MWAKHULUPIRIRADI
Yesu Ambuyathu;
Muli nazo zakezo,
Zidzatu zinanso.
Mlungu wachisomocho
Mbuye wathu ndiye,
Ati zinthu zonsezo
Nzathu mwa Iyeyo.

(Zina ndi zinanzo
Zidza kwa ifedi,
Inde mtima wakewo
Uli wokomadi.)

Mwamva Yesu m’mtimamo,
Adzanso kaŵiri,
M’mene ali nanutu
Muli ndi Chimwemwe.
Ntchito zachifundozi
Iye watha izi,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Naye tikhalebe.

Mwamva Mzimu wakewo,
Zake zimvekanso
Kugwa ngati mvulayo
Yachisomo chake.
Mzimu ndiye mphamvudi
M’moyo mwathu muno,
Mpaka tidzafikako
Komwe kuli Yesu

Post navigation

Previous: Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
Next: Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version