Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

  1. Home   »  
  2. Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

 

MWAKHULUPIRIRADI
Yesu Ambuyathu;
Muli nazo zakezo,
Zidzatu zinanso.
Mlungu wachisomocho
Mbuye wathu ndiye,
Ati zinthu zonsezo
Nzathu mwa Iyeyo.

(Zina ndi zinanzo
Zidza kwa ifedi,
Inde mtima wakewo
Uli wokomadi.)

Mwamva Yesu m’mtimamo,
Adzanso kaŵiri,
M’mene ali nanutu
Muli ndi Chimwemwe.
Ntchito zachifundozi
Iye watha izi,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Naye tikhalebe.

Mwamva Mzimu wakewo,
Zake zimvekanso
Kugwa ngati mvulayo
Yachisomo chake.
Mzimu ndiye mphamvudi
M’moyo mwathu muno,
Mpaka tidzafikako
Komwe kuli Yesu

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version