Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

  1. Home   »  
  2. Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

 

YESU Mbuyetu, mwafera
Mphulupulutu zanga,
Ndimo ndamva mund’itana,
Mutitu, Msachedwa.

Zonse za m’dziko zidzatha,
Koma za moyo m’Mwamba
Zomwe zidzakhalitsatu,
Chakatu ndi chaka.

Nyengo ifika, chenjera!
Adzakukana m’Mwamba.
Lapa zoipa zakozo,
Kuti ukaloŵe.

Post navigation

Previous: Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
Next: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version