Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

  1. Home   »  
  2. Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

 

YESU Mbuyetu, mwafera
Mphulupulutu zanga,
Ndimo ndamva mund’itana,
Mutitu, Msachedwa.

Zonse za m’dziko zidzatha,
Koma za moyo m’Mwamba
Zomwe zidzakhalitsatu,
Chakatu ndi chaka.

Nyengo ifika, chenjera!
Adzakukana m’Mwamba.
Lapa zoipa zakozo,
Kuti ukaloŵe.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version