Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

  1. Home   »  
  2. Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

 

NDICHITENJI kukapeza
Moyo? thandizeni!
Ndili wakutopa; Mzimu,
Muthandize ine.

Zonse zinathedwadi;
Yesu watha zonsezo;
Sutha ntchito, ungomvera
Mawu ake omwewo.

Iye anatsika m’Mwamba,
Anachoka kwawo,
Anafera anthu, nati:
“Ndatha zonse zawo.”

Mbuye wanga ndili kumva,
Ndikondana nanu;
Umapuma mzimu wanga,
Kwathu ndiko kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version