Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

 

M’BUKU la moyotu Mbuye,
Momwe muli, kulemba;
Tandiuzanitu Mbuye,
Ngati dzina lilimo.

Lilimo dzinali,
M’Buku lanu la moyo;
Tandiuzanitu Mbuye,
Ngati linalembedwa.

Pamene ndidza kwa Inu,
Kulapa machimowo;
M’dzandikhululukiradi,
Ndikundiyeretsanso.

Ambuye mundithandize,
Paulendo wangawu;
Pakufika kuli Inu,
Mundigwire dzanjalo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version