Chichewa Christian Hymns
Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
TAMANI mphamvu ya Yesu,
Angelo agwade;
Angelo agwade;
Tulutsanitu korona,
Mumveke, mveke, mveke,
Mveke, mveke, mveke,
Mveke Mbuyeyo!
Inu osankhidwa ake,
Owomboledwa ’Nu,
Owomboledwa ’Nu,
Tamani Mpulumutsiyo,
Anthu onse ndi mitundu
Pa dziko linotu,
Pa dziko linotu,
Am’lemekeze Mfumuyo.
Tifuna kuti komweko
Tikam’gwadire ’Ye;
Tikam’gwadire ’Ye;
Tidzayimba kosaleka.