Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 94 KHAMULO liliko

  1. Home   »  
  2. Hymn 94 KHAMULO liliko

Hymn 94 KHAMULO liliko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 94 KHAMULO liliko

 

KHAMULO liliko
Kumwambako mbuu!
Pakukhala ndi Yesu
Aimbirako:

Kwa Iye atikonda
Natsuka ’fe mbuu!
E! kukhale ulemu
Kwa Mbuyathuyu.

Onsewa ’nachimwa
Nadetsedwa bii,
Nthaŵi yino ayera
Naimbiradi:

Akhala mafumu
Kwa Mbuyathuyo,
Anawombola onse
Ndi mwaziwo pyu!

Akadakhalabe
Osaukako
Ngati Yesu sakana
Wombolatuwo.

Ndi nyimbo yabwino
Tidzamtamako,
Kuti ena pakumva
Amuyimbirenso:

Post navigation

Previous: Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
Next: Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version