Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 94 KHAMULO liliko

  1. Home   »  
  2. Hymn 94 KHAMULO liliko

Hymn 94 KHAMULO liliko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 94 KHAMULO liliko

 

KHAMULO liliko
Kumwambako mbuu!
Pakukhala ndi Yesu
Aimbirako:

Kwa Iye atikonda
Natsuka ’fe mbuu!
E! kukhale ulemu
Kwa Mbuyathuyu.

Onsewa ’nachimwa
Nadetsedwa bii,
Nthaŵi yino ayera
Naimbiradi:

Akhala mafumu
Kwa Mbuyathuyo,
Anawombola onse
Ndi mwaziwo pyu!

Akadakhalabe
Osaukako
Ngati Yesu sakana
Wombolatuwo.

Ndi nyimbo yabwino
Tidzamtamako,
Kuti ena pakumva
Amuyimbirenso:

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version