Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version