Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version