Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

 

TITAME Mlungu Wakumwamba,
Timwimbire nyimbo,
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo.

(Timwimbire nyimbo,
Timwimbire nyimbo!
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo)

Poyamba paja analenga
Zonse dziko muno,
Tsopano lomwe azisunga
Zonse zili moyo.

Tinasokera ngati nkhosa,
Moyo tinataya,
Tinakondwera ndi zoipa
Zonse tinatsata.

Komweko titasaukira,
Titafuna kufa,
Atate anatilondola
Naitana ife.

Tiyeni tizipita kwathu,
Tisasokerenso,
Tilape m’mtima kuti
tikakhale ndi Mulungu.

Post navigation

Previous: Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
Next: Hymn 25 ANGELO amayimba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version