Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

 

TITAME Mlungu Wakumwamba,
Timwimbire nyimbo,
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo.

(Timwimbire nyimbo,
Timwimbire nyimbo!
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo)

Poyamba paja analenga
Zonse dziko muno,
Tsopano lomwe azisunga
Zonse zili moyo.

Tinasokera ngati nkhosa,
Moyo tinataya,
Tinakondwera ndi zoipa
Zonse tinatsata.

Komweko titasaukira,
Titafuna kufa,
Atate anatilondola
Naitana ife.

Tiyeni tizipita kwathu,
Tisasokerenso,
Tilape m’mtima kuti
tikakhale ndi Mulungu.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version