Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

 

KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Pochimwa anthu onsewo
Nja Mlungu nzeruyi;
Adamu wachiŵiriyo
Wathetsa tchimoli.

Thupi la mwazi wathu ’li
Lochimwa kalelo,
Labweranso ku nkhondoyi,
Laposa monsemo.

Choposa nalo thupilo
Chikhale momwemu,
Chiyeretsetsa m’katimo,
Ndi Mulungu Iyeyu.

Anatikondakonda ’Ye,
Ndi Mlungu Iyeyo,
Anatifera anthu ’fe
Ndi Mulungu Iyenso.

Ndi m’munda muja chete, phee!
Pamtanda pati njo!
Anaphunzitsa’bale ’fe
Titero ifenso.

Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version