Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

 

KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Pochimwa anthu onsewo
Nja Mlungu nzeruyi;
Adamu wachiŵiriyo
Wathetsa tchimoli.

Thupi la mwazi wathu ’li
Lochimwa kalelo,
Labweranso ku nkhondoyi,
Laposa monsemo.

Choposa nalo thupilo
Chikhale momwemu,
Chiyeretsetsa m’katimo,
Ndi Mulungu Iyeyu.

Anatikondakonda ’Ye,
Ndi Mlungu Iyeyo,
Anatifera anthu ’fe
Ndi Mulungu Iyenso.

Ndi m’munda muja chete, phee!
Pamtanda pati njo!
Anaphunzitsa’bale ’fe
Titero ifenso.

Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version