Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

  1. Home   »  
  2. Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

 

MONGA zomera zonsezo
Zikula ponsepo,
Mulungu mumeretsazo,
Momwemo anawo.

Munali mwana, Yesu ’Nu
Wamng’ono kalelo,
Ndi munakula m’msinkhu ndi
Kutama ’Tatewo.

Ndi ife tinga, mbewuzo
Zomera m’mundawo;
Mumtima mutidyetsedi,
Tikule bwinomo;

Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Mumtima mwathu mbee,
Tionetsedwe konseko
A Mlungu ana ’ke.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version