Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

  1. Home   »  
  2. Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

 

KWACHA lero kwati mbee,
Tsiku la Mulunguli;
Dzuŵa liŵaliradi
Thambo ndi zapansipa
Upumira mpweyawu
Wa Mulungu konseku.

M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi
Tisonkhana teretu,
Ndi mitundu yonseyi
Tikulambireni ’Nu:
Yesu Mbuye wathuyo
Ndiye Mfumu ponsepo.

Inu Mlungu kalelo
Mutalenga zonsezi
Munapuma tsikulo;
Tipumadi ifenso.
Mommo tilandiratu
Zopumitsa mtimawu.

Yesu munadzukanso
M’manda lero lomwetu;
Ntchito munayambayo
Yakudzutsa anthu ’fe,
Kuti ndi mitimayi
Tigwirebe ntchitozi.

Post navigation

Previous: Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
Next: Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version