Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

 

MUMZINDA wa Mulungu
Moyera mulimo,
Ndiye amathu omwe
Olera ifewo;
Mitima yathu yomwe
Ikondwereratu,
Nikhala nawo Mzinda
Wakukongolawu.

Akondwerera anthu Zokoma zonsezi
Za midzi ya padziko
Lapansi lonseli;
Mtendere wake koma
Wa Mzinda wathuwo
Upambanditsa zonse
Zapansi pomwepo.

Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mlungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzoza mutu tho!

Post navigation

Previous: Hymn 328 KULIBE vuto
Next: Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version