Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

 

MUMZINDA wa Mulungu
Moyera mulimo,
Ndiye amathu omwe
Olera ifewo;
Mitima yathu yomwe
Ikondwereratu,
Nikhala nawo Mzinda
Wakukongolawu.

Akondwerera anthu Zokoma zonsezi
Za midzi ya padziko
Lapansi lonseli;
Mtendere wake koma
Wa Mzinda wathuwo
Upambanditsa zonse
Zapansi pomwepo.

Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mlungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzoza mutu tho!

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version