Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

  1. Home   »  
  2. Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

 

KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
Werengani Mawu masiku onsewo.
Uthenga omwe ali akufoka,
Madalitso ake ufunefunebe.

Khalani woyera, dziko laipadi;
Pemphera kolimba kwa Yesu
Mbuyathu.
Yang’anitsa Yesu ndi kumutsatira,
Kuti anthu ena aonenso Iye.

Khalatu woyera, akutsogozetu;
Usamtsogolere munjira zakozo.
Pokondwa ndi m’nsoni tsata Ambuyako
Khulupira Yesu ndi Mawu akewo.

Khalatu woyera, khalatu wofatsa;
Alilamulire ganizo lakolo.
Utatsogozedwa ndi Mzimu wakeyo,
Msanga udzagwira m’Mwamba ntchito yake.

Post navigation

Previous: Hymn 263 AMBUYE mundisunge
Next: Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version