Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

  1. Home   »  
  2. Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

 

KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
Werengani Mawu masiku onsewo.
Uthenga omwe ali akufoka,
Madalitso ake ufunefunebe.

Khalani woyera, dziko laipadi;
Pemphera kolimba kwa Yesu
Mbuyathu.
Yang’anitsa Yesu ndi kumutsatira,
Kuti anthu ena aonenso Iye.

Khalatu woyera, akutsogozetu;
Usamtsogolere munjira zakozo.
Pokondwa ndi m’nsoni tsata Ambuyako
Khulupira Yesu ndi Mawu akewo.

Khalatu woyera, khalatu wofatsa;
Alilamulire ganizo lakolo.
Utatsogozedwa ndi Mzimu wakeyo,
Msanga udzagwira m’Mwamba ntchito yake.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version