Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

 

WANENA ndi Yesu,
Mawu onse awa;
Mfumu yamtendere,
Yalonjeza kuti:

“Sindim’tulutsa
sindidzam ‘taya;
Wakudza kwa Ine
Sindim’tulutsa,
sindidzam’taya
Wakudza kwa Ine.”

“Mfulu ndi kapolo,
Adzetu kwa Ine;”
Wanena ndi Yesu,
Mawu onse awa.

Onse akulapa,
Adzawona mwayi;
Ndipo adzayimba,
Pamodzi ndi Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version