Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
Next: Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version