Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version