Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.

  1. Home   »  
  2. Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.

Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.

 

YESU atiuza tiŵale ’fe.
Monga nyali m’mdima tiunike mbee!
Pansi pali mdima ŵalanitu,
Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.

Yesu atiuza tiyambemo,
Ationa bwino ndi kuŵalako;
Ayang’ana pansi poŵala ’fe,
Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.

Yesu atiuza tiŵale pa
Anthu ali m’mdima osaukawa;
Tiŵalire onse, tonsefetu,
Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version