Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

  1. Home   »  
  2. Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

 

MKRISTU, ulimbike
M’ntchito yakeyo;
Yesu anafera
Anthu akewo.

Mphamvu zathu zonse
Tionetsenso,
Kuti kudziŵike
Tili akewo.

Mtima wakufatsa
Amakondako;
Ndipo anthu onse
Angatengero.

Mapemphero athu
Tikakwezebe,
Dzina lake lomwe
Tiyamike ’fe.

Limbikani nonse
Mpaka imfayo.
Ndipo Mfumu yathu
Idzakondwatu.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version