Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

 

ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
Unikani! Unikani!
Alikumwazika
Mungawalanditse,
Unikani! Unikaní!

Tumizani kuunikako,
Kuwoneketu kwa onsewo;
Tumizani kuunikako,
Nthawi zonsedi kuwaletu.

Tamva aku
Makedon’yako atero,
Unikani! Unikani!
Tititu, Ambuye tizinka komweko,
Unikani! Unikani!

Tisaleme pakuchita zabwinozi,
Unikani! Unikani!
Tidziunjikire ngale za Kumwamba,
Unikani! Unikani!

Exit mobile version